Zomwe wayankhula Bon Kalindo Lero pa 13 July 2024 pa nkhani ya kutuluka kwa UTM mu Tonse Alliance
27,116
Published 2024-07-12
All Comments (21)
-
UTM back to DPP never we r on our own🔥🔥🔥🔥🔥
-
Koma fact ndiyakut apapa a UTM mwaphunziladi angakhale achedwa koma this is brave idea , tili ku mbuyo kwanu .
-
UTM should first stand on its own. Build the party
-
❤❤❤This guy he's genius Ndipo amati fightiler kwambiri 🔥
-
Uyuyu a Malawi ambr mmamupeputsa ,.koma nthw idzakwana ubwino wake muzaudziwa Chitsime chimaoneka chokuya madzi akaphwa
-
From town centre Mitchell's capetown bon ndimakudyadilan kwambili God ahead u bro
-
Asiyeni a UTM apange zomwe agwirizana
-
Utm bwelenani ku dpp kuti udzamange amene anapha chilima
-
Ndale zokha zokha,mwasiya masewero abwino, ndalama iwonongesa mbiri
-
Kalindo salimoyesa 🎉🎉🎉🎉🎉🎉👍👍👍👍💯
-
Mumakwana Mr DC
-
Kkkkkk Manganya adali Yudasi zoona, bwato satsilana pakati pa nyanja kkkkkk
-
Nkhani ikhale UTM , AFORD ndi UDF apange alliance, president achoke ku UTM ndekuti azapeza ma vote Ku north , central pang'ono koma ochuluka ku southern nde kuti azaiphula bho bho
-
Ku dpp tikataniko? Chilima anatulukako ndipo sanabwelere mpaka kufa kwake ndiye ife tufuna mufuna mzimu wake utikanthe?
-
Iwe ndi machine🔥🔥🔥
-
The DC is right
-
UTM ISAPHATIKIZANE NDI DPP CHIFUKWA MKAZI WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POTHAWA MOTO KU SODOMU..PAMENE NGELO WA AMBUYE ANAWAUZA KUTI ALIYENSE ASAYANG'ANE MBUYO. KOMA MKAZI WAKE WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POGANIZIRA MOWA WAKE WOMWE ANKAPHIKA KUSOMUKO NKUMAGULITSA. IYEO ANASANDUKA CHULU CHA MCHERE. SO UTM NSO MUKAPHATIKANA NDI DPP MUSANDUKA CHULU CHA MCHERE.MUKHALA STUCK AND DORMANT DEAD WOOD .!!!
-
Propaganda at its peak. Ife anthu osauka takana kuti ndiwe president wathu
-
UTM welcome back to DPP family
-
Ubwino wake ovota ndife, and kalikonse kochitika pansi pathambo Mulungu amachionetsa poyera